1 Timoteyo 3:5 - Buku Lopatulika5 Koma ngati munthu sadziwa kuweruza nyumba ya iye yekha, adzasunga bwanji Mpingo wa Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma ngati munthu sadziwa kuweruza nyumba ya iye yekha, adzasunga bwanji Mpingo wa Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ngati munthu sadziŵa kuyendetsa bwino banja lake, nanga angasunge bwanji Mpingo wa Mulungu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 (Ngati munthu sadziwa kusamala banja lake lomwe, angathe bwanji kusamala mpingo wa Mulungu?) Onani mutuwo |