Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Timoteyo 3:10 - Buku Lopatulika

10 Koma iwonso ayamba ayesedwe; pamenepo atumikire, akakhala opanda chifukwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Koma iwonso ayamba ayesedwe; pamenepo atumikire, akakhala opanda chifukwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Iwonso ayambe ayesedwa, ndipo pambuyo pake, ngati alibe chokayikitsa, ndiye asenze udindo wa atumiki.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ayambe ayesedwa kaye, ndipo ngati palibe kanthu kowatsutsa, aloleni akhale atumiki.

Onani mutuwo Koperani




1 Timoteyo 3:10
9 Mawu Ofanana  

amenenso adzakukhazikitsani inu kufikira chimaliziro, kuti mukhale opanda chifukwa m'tsiku la Ambuye wathu Yesu Khristu.


koma tsopano anakuyanjanitsani m'thupi lake mwa imfayo, kukaimika inu oyera, ndi opanda chilema ndi osatsutsika pamaso pake;


Pakuti iwo akutumikira bwino adzitengera okha mbiri yabwino, ndi kulimbika kwakukulu m'chikhulupiriro cha mwa Khristu Yesu.


Ndipo kuyenera woyang'anira akhale wopanda chilema, mwamuna wa mkazi mmodzi, wodzisunga, wodziletsa, wolongosoka, wokonda kuchereza alendo, wokhoza kuphunzitsa;


Asakhale wophunza, kuti podzitukumula ungamgwere mlandu wa mdierekezi.


Usafulumira kuika manja pa munthu aliyense, kapena usayanjana nazo zoipa za eni; udzisunge wekha woyera mtima.


Okondedwa, musamakhulupirira mzimu uliwonse, koma yesani mizimu ngati ichokera mwa Mulungu: popeza aneneri onyenga ambiri anatuluka kulowa m'dziko lapansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa