1 Timoteyo 2:8 - Buku Lopatulika8 Chifukwa chake ndifuna kuti amunawo apemphere pamalo ponse, ndi kukweza manja oyera, opanda mkwiyo ndi makani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Chifukwa chake ndifuna kuti amunawo apemphere pamalo ponse, ndi kukweza manja oyera, opanda mkwiyo ndi makani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ndikufuna kuti paliponse amuna popemphera azikweza manja ao kwa Mulungu momchitira ulemu, mopanda mkwiyo kapena kukangana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Choncho ndikufuna kuti paliponse popemphera, amuna azikweza manja awo kwa Mulungu mopanda mkwiyo kapena kukangana. Onani mutuwo |