1 Timoteyo 2:6 - Buku Lopatulika6 amene anadzipereka yekha chiombolo m'malo mwa onse; umboni m'nyengo zake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 amene anadzipereka yekha chiombolo m'malo mwa onse; umboni m'nyengo zake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Iyeyo adadzipereka kuti akhale momboli wa anthu onse. Umenewu unali umboni umene udaperekedwa pa nthaŵi yake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iyeyu anadzipereka kukhala dipo lowombolera anthu onse. Umenewu ndi umboni umene waperekedwa mu nthawi yake yoyenera. Onani mutuwo |