Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Timoteyo 2:13 - Buku Lopatulika

13 Pakuti Adamu anayamba kulengedwa, pamenepo Heva;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Pakuti Adamu anayamba kulengedwa, pamenepo Heva;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Paja Adamu ndiye adaayambira kulengedwa, pambuyo pake Heva.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Pakuti Adamu ndiye anayamba kupangidwa kenaka Hava.

Onani mutuwo Koperani




1 Timoteyo 2:13
7 Mawu Ofanana  

Mulungu ndipo adalenga munthu m'chifanizo chake, m'chifanizo cha Mulungu adamlenga iye; adalenga iwo mwamuna ndi mkazi.


Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.


Ndipo nthitiyo anaichotsa Yehova Mulungu mwa Adamu anaipanga mkazi, ndipo ananka naye kwa Adamu.


Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.


Kwa mkaziyo ndipo anati, Ndidzachulukitsa kusauka kwako ndi potenga mimba pako; udzasauka pakubala: udzakhumba mwamuna wako, ndipo iye adzakulamulira iwe.


Ndipo mwamuna anamutcha dzina la mkazi wake, Heva; chifukwa ndiye amake wa amoyo onse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa