Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Timoteyo 2:12 - Buku Lopatulika

12 Koma sindilola ine kuti mkazi aphunzitse, kapena kulamulira mwamuna; komatu akhale chete.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Koma sindilola ine kuti mkazi aphunzitse, kapena kulamulira mwamuna; komatu akhale chete.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Sindilola kuti mkazi aziphunzitsa kapena kukhala ndi ulamuliro pa amuna. Mkazi kwake nkukhala chete.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ine sindikulola kuti amayi aziphunzitsa kapena kulamulira amuna; koma akhale chete.

Onani mutuwo Koperani




1 Timoteyo 2:12
2 Mawu Ofanana  

Akazi akhale chete mu Mipingo. Pakuti sikuloledwa kwa iwo kulankhula. Koma akhale omvera, monganso chilamulo chinena.


akhale odziletsa, odekha, ochita m'nyumba mwao, okoma, akumvera amuna a iwo okha, kuti mau a Mulungu angachitidwe mwano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa