1 Timoteyo 2:10 - Buku Lopatulika10 komatu (umo mokomera akazi akuvomereza kulemekeza Mulungu), mwa ntchito zabwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 komatu (umo mokomera akazi akuvomereza kulemekeza Mulungu), mwa ntchito zabwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Kwenikweni adzikongoletse ndi ntchito zabwino, monga ayenera kuchitira akazi amene amati ndi opembedza Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Koma adzikongoletse ndi ntchito zabwino zoyenera mayi wopembedza Mulungu. Onani mutuwo |