1 Timoteyo 1:7 - Buku Lopatulika7 pofuna kukhala aphunzitsi a malamulo ngakhale sadziwitsa zimene azinena, kapena azilimbikirazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 pofuna kukhala aphunzitsi a malamulo ngakhale sadziwitsa zimene azinena, kapena azilimbikirazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Iwo amafuna kukhala aphunzitsi a Malamulo a Mulungu, chonsecho samvetsa zimene iwo omwe akunena kapena zimene akufuna kutsimikiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iwo amafuna kukhala aphunzitsi amalamulo, koma sadziwa zimene akunena, kapena zimene akufuna kutsimikiza. Onani mutuwo |