1 Timoteyo 1:6 - Buku Lopatulika6 zimenezo, ena pozilambalala anapatukira kutsata mau opanda pake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 zimenezo, ena pozilambalala anapatukira kutsata mau opanda pake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Anthu ena adapatuka pa zimenezi, ndipo adasokera nkumatsata nkhani zopanda pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Anthu ena anapatuka pa zimenezi ndipo anatsata nkhani zopanda tanthauzo. Onani mutuwo |