Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Timoteyo 1:6 - Buku Lopatulika

6 zimenezo, ena pozilambalala anapatukira kutsata mau opanda pake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 zimenezo, ena pozilambalala anapatukira kutsata mau opanda pake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Anthu ena adapatuka pa zimenezi, ndipo adasokera nkumatsata nkhani zopanda pake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Anthu ena anapatuka pa zimenezi ndipo anatsata nkhani zopanda tanthauzo.

Onani mutuwo Koperani




1 Timoteyo 1:6
9 Mawu Ofanana  

Nanga muyesa bwanji? Ngati munthu ali nazo nkhosa makumi khumi, ndipo ikasokera imodzi ya izo, kodi saleka zija makumi asanu ndi anai mphambu zisanu ndi zinai, napita kumapiri, kukafuna yosokerayo?


pakuti adayamba ena kupatuka ndi kutsata Satana.


ndiwo amene adasokera kunena za choonadi, ponena kuti kuuka kwa akufa kwachitika kale, napasula chikhulupiriro cha ena.


pakuti Dema wandisiya ine, atakonda dziko lino lapansi, napita ku Tesalonika; Kresike ku Galatiya, Tito ku Dalamatiya.


Pakuti alipo ambiri osamvera mau, olankhula zopanda pake, ndi onyenga, makamaka iwo akumdulidwe,


koma pewa mafunso opusa, ndi mawerengedwe a mibadwo, ndi ndeu, ndi makani a pamalamulo; pakuti sizipindulitsa, ndipo zili zachabe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa