1 Timoteyo 1:11 - Buku Lopatulika11 monga mwa Uthenga Wabwino wa ulemerero wa Mulungu wolemekezeka, umene anandisungitsa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 monga mwa Uthenga Wabwino wa ulemerero wa Mulungu wolemekezeka, umene anandisungitsa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chiphunzitso choonacho chimapezeka mu Uthenga Wabwino wonena za ulemerero wa Mulungu wolemekezeka, umene Iye mwini adandisungiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Chiphunzitso chimene chimagwirizana ndi Uthenga Wabwino wonena za ulemerero wa Mulungu wodala, umene Iye mwini anandisungitsa. Onani mutuwo |