Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 25:40 - Buku Lopatulika

40 Ndipo anyamata a Davide pakufika kwa Abigaile ku Karimele, analankhula naye, nati, Davide anatitumiza kwa inu, kukutengani, mukhale mkazi wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Ndipo anyamata a Davide pakufika kwa Abigaile ku Karimele, analankhula naye, nati, Davide anatitumiza kwa inu, kukutengani, mukhale mkazi wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Anyamata a Davide atafika kwa Abigaile ku Karimele, adamuuza kuti “Mfumu Davide watituma kuti tikutengeni, mukakhale mkazi wake.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Anyamata a Davide atafika ku Karimeli anawuza Abigayeli kuti, “Davide watituma kwa iwe kuti tikutenge ukhale mkazi wake.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 25:40
5 Mawu Ofanana  

Taonani, Rebeka ali pamaso pako, mtenge ndi kumuka, akhale mkazi wa mwana wa mbuyako, monga wanena Yehova.


Mkazi wodekha agwiritsa ulemu; aukali nagwiritsa chuma.


Ndipo pamene Davide anamva kuti Nabala adamwalira, iye anati, Alemekezedwe Yehova, amene anaweruza mlandu wa mtonzo wanga wochokera ku dzanja la Nabala, naletsa mnyamata wake pa choipa; ndipo Yehova anabwezera pamutu pa Nabala choipa chake. Ndipo Davide anatumiza wokamfunsira Abigaile, zakuti amtengere akhale mkazi wake.


Ndipo iye ananyamuka, nawerama nkhope yake pansi, nati, Onani, mdzakazi wanu ali kapolo wakusambitsa mapazi a anyamata a mbuye wanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa