1 Samueli 25:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo pamene Davide anamva kuti Nabala adamwalira, iye anati, Alemekezedwe Yehova, amene anaweruza mlandu wa mtonzo wanga wochokera ku dzanja la Nabala, naletsa mnyamata wake pa choipa; ndipo Yehova anabwezera pamutu pa Nabala choipa chake. Ndipo Davide anatumiza wokamfunsira Abigaile, zakuti amtengere akhale mkazi wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo pamene Davide anamva kuti Nabala adamwalira, iye anati, Alemekezedwe Yehova, amene anaweruza mlandu wa mtonzo wanga wochokera ku dzanja la Nabala, naletsa mnyamata wake pa choipa; ndipo Yehova anabwezera pamutu pa Nabala choipa chake. Ndipo Davide anatumiza wokamfunsira Abigaile, zakuti amtengere akhale mkazi wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Tsono Davide atamva kuti Nabala wafa, adati, “Atamandike Chauta amene walipsira chipongwe chimene adandichita Nabala, ndipo wandiletsa ine mtumiki wake kuti ndisachite choipa. Chauta wabwezera pamutu pa Nabala ntchito zake zoipa.” Tsono Davide adatuma anyamata ake kukafunsira mbeta Abigaile kuti akhale mkazi wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Pamene Davide anamva kuti Nabala wamwalira, iye anati, “Alemekezeke Yehova, walipsira Nabala chipongwe chimene anandichita ndipo anandiletsa ine mtumiki wake kuti ndisachite choyipa. Yehova wabwezera pamutu pa Nabala choyipa chimene iye anachita.” Kenaka Davide anatumiza mawu kwa Abigayeli, kumupempha kuti akhale mkazi wake. Onani mutuwo |