Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Samueli 25:37 - Buku Lopatulika

37 Tsono m'mawa vinyo atamchokera Nabala, mkazi wake anamuuza zimenezi; ndipo mtima wake unamyuka m'kati mwake, iye nasanduka ngati mwala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Tsono m'mawa vinyo atamchokera Nabala, mkazi wake anamuuza zimenezi; ndipo mtima wake unamyuka m'kati mwake, iye nasanduka ngati mwala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 M'maŵa mwake, m'maso mwa Nabala mutayera, mkazi wakeyo adamuuza zonse. Pomwepo Nabala mtima wake udaima, ndipo thupi lidangoti gwa ngati mwala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Tsono mmawa, mowa utamuchoka Nabala, mkazi wake anamuwuza zonse. Pomwepo mtima wake unaleka kugunda ndipo unawuma gwaa ngati mwala.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 25:37
7 Mawu Ofanana  

Yehova adzakukanthani ndi misala, ndi khungu, ndi kuzizwa mumtima;


Mulungu alange adani a Davide, ndi kuonjezerapo, ngati ndisiyapo kufikira kuunika kwa m'mawa, kanthu konse ka iye, kangakhale kamwana kamphongo.


Pakuti ndithu, Pali Yehova Mulungu wa Israele, amene anandiletsa lero kusapweteka iwe, ukadapanda kufulumira kubwera kundichingamira, zoonadi sindikadasiyira Nabala kufikira kutacha kanthu konse, ngakhale mwana wamwamuna mmodzi.


Ndipo Abigaile anafika kwa Nabala; ndipo, onani, anali ndi madyerero m'nyumba mwake, monga madyerero a mfumu; ndi mtima wa Nabala unasekera kwambiri m'kati mwake, pakuti analedzera kwambiri; m'mwemo uyo sadamuuze kanthu konse, kufikira kutacha.


Ndipo kunali, atapita masiku khumi, Yehova anamkantha Nabala, nafa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa