Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Samueli 25:35 - Buku Lopatulika

35 Chomwecho Davide analandira m'dzanja lake zimene iye anamtengera; nanena naye, Ukwere kwanu mumtendere; ona, ndamvera mau ako, ndavomereza nkhope yako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Chomwecho Davide analandira m'dzanja lake zimene iye anamtengera; nanena naye, Ukwere kwanu mumtendere; ona, ndamvera mau ako, ndavomereza nkhope yako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Motero Davide adalandira kwa mkaziyo zimene adaamtengera, namuuza kuti, “Pitani kunyumba kwanu ndi mtendere. Mau anu ndaŵamva ndipo zopempha ndavomera.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Ndipo Davide analandira kwa mayiyo zimene anamutengera ndipo anati, “Pitani kwanu mu mtendere. Ine ndamva mawu anu ndipo ndavomera zimene mwapempha.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 25:35
9 Mawu Ofanana  

Ndipo anati kwa iye, Taona, ndikuvomereza iwe pamenepanso kuti sindidzaononga mzinda uwu umene wandiuza.


Ndipo mfumu inanena naye, Muka ndi mtendere. Chomwecho ananyamuka, nanka ku Hebroni.


Ndipo ananena naye, Pita mumtendere. Ndipo anachoka, nayenda kanthawi.


Nanga kwa Iye wosasamalira nkhope za akalonga, wosasiyanitsa pakati pa wolemera ndi wosauka? Pakuti onsewo ndiwo ntchito ya manja ake.


Mau oyenera a pa nthawi yake akunga zipatso zagolide m'nsengwa zasiliva.


Ndipo Iye anati kwa mkaziyo, Chikhulupiriro chako chakupulumutsa iwe; muka ndi mtendere.


Ndipo Iye anati kwa iyeyu, Mwana wanga, chikhulupiriro chako chakupulumutsa iwe; muka ndi mtendere.


Pamenepo Eli anayankha nati, Pita ndi mtendere; ndipo Mulungu wa Israele akupatse chopempha chako unachipempha kwa Iye.


Ndipo Yonatani ananena kwa Davide, Muka mumtendere, popeza tonsefe tinalumbira m'dzina la Yehova, kuti, Yehova adzakhala pakati pa ine ndi iwe, ndi pakati pa mbeu yako, nthawi zamuyaya. Ndipo iye ananyamuka nachoka; koma Yonatani anamuka kumzinda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa