1 Samueli 25:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo mphatso iyi mdzakazi wanu ndatengera mbuye wanga, ipatsidwe kwa anyamata akutsata mbuye wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo mphatso iyi mdzakazi wanu ndatengera mbuye wanga, ipatsidwe kwa anyamata akutsata mbuye wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Pepani, nazi mphatsozi zimene mdzakazi wanune ndabwera nazo kwa inu mbuyanga, kuti zipatsidwe kwa anthu muli nawoŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Choncho, nazi mphatso zimene mdzakazi wanu ndabwera nazo kwa mbuye wanga kuti zipatsidwe kwa anyamata amene muli nawo. Onani mutuwo |