1 Samueli 25:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo atagwadira pa mapazi ake anati, Pa ine, mbuye wanga, pa ine pakhale uchimowo; ndipo mulole mdzakazi wanu alankhule m'makutu anu, nimumvere mau a mdzakazi wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo atagwadira pa mapazi ake anati, Pa ine, mbuye wanga, pa ine pakhale uchimowo; ndipo mulole mdzakazi wanu alankhule m'makutu anu, nimumvere mau a mdzakazi wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Ali chigonere choncho ku mapazi a Davide adati, “Mbuyanga, mlandu ugwere ine ndekha basi. Chonde mulole mdzakazi wanune kuti ndilankhule nanu, ndipo mumve mau anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Ali chigonere choncho pa mapazi a Davide anati, “Mbuye wanga, kulakwa kukhale pa ine ndekha. Chonde lolani kuti mdzakazi wanune ndiyankhule nanu, ndipo mumve mawu a ine mdzakazi wanu. Onani mutuwo |