1 Samueli 18:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo akazi anathirirana mang'ombe m'kuimba kwao, nati, Saulo anapha zikwi zake, koma Davide zikwi zake zankhani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo akazi anathirirana mang'ombe m'kuimba kwao, nati, Saulo anapha zikwi zake, koma Davide zikwi zake zankhani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Akaziwo ankapolokezana akukondwerera namati, “Saulo wapha zikwi inde, koma Davide wapha zikwi khumikhumi!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Amayiwo ankalandizana nyimbo mokondwera namati: “Sauli wapha 1,000, Koma Davide wapha miyandamiyanda.” Onani mutuwo |