1 Samueli 18:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Saulo anaopa Davide chifukwa Yehova anali naye, koma adamchokera Saulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Saulo anaopa Davide chifukwa Yehova anali naye, koma adamchokera Saulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pambuyo pake Saulo adayamba kuwopa Davide, chifukwa choti tsopano Chauta anali ndi Davide, kumsiya iyeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Pambuyo pake Sauli amamuopa Davide chifukwa Yehova anali ndi Davideyo, nʼkumusiya Sauli. Onani mutuwo |
Ndipo Samuele ananena ndi Saulo, Wandivutiranji kundikweretsa kuno? Saulo nayankha, Ndilikusautsika kwambiri, pakuti Afilisti aponyana nkhondo ndi ine, ndipo Mulungu anandichokera, osandiyankhanso, kapena ndi aneneri, kapena ndi maloto; chifukwa chake ndakuitanani, kuti mundidziwitse chimene ndiyenera kuchita.