1 Petro 5:3 - Buku Lopatulika3 osati monga ochita ufumu pa iwo a udindo wanu, koma okhala zitsanzo za gululo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 osati monga ochita ufumu pa iwo a udindo wanu, koma okhala zitsanzo za gululo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Musakhale ngati mafumu odzikuza potsogolera anthu amene muyenera kuŵayang'anira, koma onetsani chitsanzo chabwino kwa nkhosazo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Musakhale ngati mafumu pa amene mukuwayangʼanira, koma mukhale chitsanzo kwa gululo. Onani mutuwo |