Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Petro 4:9 - Buku Lopatulika

9 mucherezane wina ndi mnzake, osadandaula:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 mucherezane wina ndi mnzake, osadandaula:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Poyenderana, muzisamalirana bwino mosadandaula.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Muzisamalirana wina ndi mnzake osamanyinyirika.

Onani mutuwo Koperani




1 Petro 4:9
11 Mawu Ofanana  

Atatha kumwetsa iye, anati, Ndidzatungiranso ngamira zako, mpaka zitamwa zonse.


Patsani zosowa oyera mtima; cherezani aulendo.


Gayo, mwini nyumba wolandira ine, ndi Mpingo wonse wa Ambuye, akupereka moni. Erasto, ndiye woyang'anira mzinda, akupereka moni, ndiponso Kwarto mbaleyo.


Yense achite monga anatsimikiza mtima, si mwa chisoni kapena mokakamiza, pakuti Mulungu akonda wopereka mokondwerera.


Chitani zonse kopanda madandaulo ndi makani,


Ndipo kuyenera woyang'anira akhale wopanda chilema, mwamuna wa mkazi mmodzi, wodzisunga, wodziletsa, wolongosoka, wokonda kuchereza alendo, wokhoza kuphunzitsa;


komatu wokonda kuchereza alendo, wokonda zokoma, wodziweruza, wolungama, woyera mtima, wodziletsa;


koma wopanda kudziwa mtima wako sindinafune kuchita kanthu; kuti ubwino wako usakhale monga mokakamiza, komatu mwaufulu.


Koma musaiwale kuchitira chokoma ndi kugawira ena; pakuti nsembe zotere Mulungu akondwera nazo.


Musaiwale kuchereza alendo; pakuti mwa ichi ena anachereza angelo osachidziwa.


Musaipidwe wina ndi mnzake, abale, kuti mungaweruzidwe. Taonani, woweruza aima pakhomo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa