1 Petro 4:4 - Buku Lopatulika4 m'menemo ayesa nchachilendo kuti simuthamanga nao kufikira kusefukira komwe kwa chitayiko, nakuchitirani mwano; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 m'menemo ayesa nchachilendo kuti simuthamanga nao kufikira kusefukira komwe kwa chitayiko, nakuchitirani mwano; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Anthu akunja amadabwa tsopano poona kuti mwaleka kuthamangira nao zoipitsitsa zimene iwo amachita mosadziletsa konse. Nchifukwa chake amalalata. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Anthu osapembedza amadabwa pamene simuthamangira nawo kuchita zoyipitsitsazi, nʼchifukwa chake amakuchitani chipongwe. Onani mutuwo |