1 Petro 4:2 - Buku Lopatulika2 kuti nthawi yotsalira simukakhalenso ndi moyo m'thupi kutsata zilakolako za anthu, koma chifuniro cha Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 kuti nthawi yotsalira simukakhalenso ndi moyo m'thupi kutsata zilakolako za anthu, koma chifuniro cha Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Choncho, pa nthaŵi yatsala yoti mukhale pansi pano, simudzatsatanso zilakolako za anthu, koma mudzatsata kufuna kwa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Chifukwa cha ichi, iwo sakhalanso moyo wawo akuchita zofuna za matupi awo, koma amachita chifuniro cha Mulungu. Onani mutuwo |