1 Petro 3:3 - Buku Lopatulika3 Amene kukometsera kwanu kusakhale kwa kunja, kuluka tsitsi ndi kuvala za golide, kapena kuvala chovala; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Amene kukometsera kwanu kusakhale kwa kunja, kuluka tsitsi ndi kuvala za golide, kapena kuvala chovala; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kudzikongoletsa kwanu kusangokhala kwa maonekedwe akunja pakuluka tsitsi, ndi kuvala zamakaka zagolide ndi zovala zamtengowapatali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kudzikongoletsa kwanu kusakhale kwa maonekedwe akunja, monga kuluka tsitsi ndi kuvala zokometsera zagolide ndi zovala zamberewere. Onani mutuwo |