1 Petro 2:4 - Buku Lopatulika4 amene pakudza kwa Iye, mwala wamoyo, wokanidwatu ndi anthu, koma ndi Mulungu wosankhika, waulemu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 amene pakudza kwa Iye, mwala wamoyo, wokanidwatu ndi anthu, koma ndi Mulungu wosankhika, waulemu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Bwerani kwa Iye amene ali mwala wamoyo womwe anthu adaukana, koma Mulungu adausankha kuti ngwamtengowapatali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pamene mukubwera kwa Iye, amene ndi Mwala wa moyo, umene anthu anawukana, koma Mulungu anawusankha kuti ndi wa mtengowapatali, Onani mutuwo |