Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Petro 2:3 - Buku Lopatulika

3 ngati mwalawa kuti Ambuye ali wokoma mtima;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 ngati mwalawa kuti Ambuye ali wokoma mtima;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 popeza kuti mwachilaŵadi chifundo cha Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 pakuti tsopano mwalawadi kuti Ambuye ndi wabwino.

Onani mutuwo Koperani




1 Petro 2:3
8 Mawu Ofanana  

Mfumu imene ya ulemerero ndani? Yehova wamphamvu ndi wolimba, Yehova wolimba kunkhondo.


Talawani, ndipo onani kuti Yehova ndiye wabwino; wodala munthuyo wakukhulupirira Iye.


Mudzakhutitsa moyo wanga ngati ndi mafuta ndi zonona; ndipo pakamwa panga ndidzakulemekezani ndi milomo yakufuula mokondwera.


ndipo iwo akudziwa dzina lanu adzakhulupirira Inu; pakuti, Inu Yehova, simunawasiye iwo akufuna Inu.


Ngati maula pakati pa mitengo ya m'nkhalango, momwemo wokondedwa wanga pakati pa ana aamuna. Ndinakondwa pakukhala pa mthunzi wake, zipatso zake zinatsekemera m'kamwa mwanga.


Pakuti ukoma wake ndi waukulu ndithu, ndi kukongola kwake nkwakukulu ndithu! Tirigu adzakometsera anyamata, ndi vinyo watsopano anamwali.


Koma pamene kukoma mtima, ndi chikondi cha pa anthu, cha Mpulumutsi wathu Mulungu zidanoneka,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa