Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Petro 1:9 - Buku Lopatulika

9 ndi kulandira chitsiriziro cha chikhulupiriro chanu, ndicho chipulumutso cha moyo wanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 ndi kulandira chitsiriziro cha chikhulupiriro chanu, ndicho chipulumutso cha moyo wanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Pakutero mukupata mphotho ya chikhulupiriro, ndiye kuti chipulumutso chanu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Motero mukulandira mphotho ya chikhulupiriro chanu, ndiyo chipulumutso cha moyo wanu.

Onani mutuwo Koperani




1 Petro 1:9
4 Mawu Ofanana  

Koma tsopano, pamene munamasulidwa kuuchimo, ndi kukhala akapolo a Mulungu, muli nacho chobala chanu chakufikira chiyeretso, ndi chimaliziro chake moyo wosatha.


Iwo onse adamwalira m'chikhulupiriro, osalandira malonjezano, komatu adawaona ndi kuwalankhula kutali, navomereza kuti ali alendo ndi ogonera padziko.


Mwa ichi, mutavula chinyanso chonse ndi chisefukiro cha choipa, landirani ndi chifatso mau ookedwa mwa inu, okhoza kupulumutsa moyo wanu.


imene inakhala yosamvera kale, pamene kuleza mtima kwa Mulungu kunalindira, m'masiku a Nowa, pokhala m'kukonzeka chingalawa, m'menemo owerengeka, ndiwo amoyo asanu ndi atatu, anapulumutsidwa mwa madzi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa