1 Petro 1:4 - Buku Lopatulika4 kuti tilandire cholowa chosavunda ndi chosadetsa ndi chosafota, chosungikira mu Mwamba inu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 kuti tilandire cholowa chosavunda ndi chosadetsa ndi chosafota, chosungikira m'Mwamba inu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 kuti tidzalandira ngati choloŵa zokoma zosaonongeka, zosaipitsidwa, ndi zosafota, zimene Mulungu akukusungirani Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 kuti tidzalandire chuma chomwe sichingawonongeke, kuyipitsidwa kapena kufota. Chuma chimenechi akukusungirani kumwamba. Onani mutuwo |