Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 9:9 - Buku Lopatulika

9 ndi abale ao monga mwa mibadwo yao mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu kudza asanu ndi mmodzi. Onsewa ndiwo akulu a nyumba za makolo ao m'nyumba za makolo ao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 ndi abale ao monga mwa mibadwo yao mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu kudza asanu ndi mmodzi. Onsewa ndiwo akulu a nyumba za makolo ao m'nyumba za makolo ao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Ndipo mabanja ao potsata mibadwo yao analipo 956. Onse amene alembedwa pamwambapaŵa anali atsogoleri a mabanja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Anthu ochokera ku Benjamini monga analembedwera mwa mibado yawo, analipo 956. Anthu onsewa anali atsogoleri a mabanja awo.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 9:9
2 Mawu Ofanana  

ndi Ibineya mwana wa Yerohamu, ndi Ela mwana wa Uzi, mwana wa Mikiri, ndi Mesulamu mwana wa Sefatiya, mwana wa Reuwele, mwana wa Ibineya,


Ndi wotsatana naye Gabai, Salai, mazana asanu ndi anai mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa