1 Mbiri 9:6 - Buku Lopatulika6 Ndi a ana a Zera: Yeuwele ndi abale ao mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi anai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndi a ana a Zera: Yeuwele ndi abale ao mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi anai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 A kwa Azera anali aŵa: Yeuwele ndi achibale ao, onse pamodzi 690. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 A banja la Zera: Yeueli. Anthu ochokera ku Yuda analipo 690. Onani mutuwo |