1 Mbiri 9:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo mu Yerusalemu munakhala a ana a Yuda, ndi a ana a Benjamini, ndi a ana a Efuremu ndi Manase: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo m'Yerusalemu munakhala a ana a Yuda, ndi a ana a Benjamini, ndi a ana a Efuremu ndi Manase: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Anthu ena a ku Yuda, Benjamini, Efuremu ndi Manase amene ankakhala ku Yerusalemu anali motere: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Anthu a ku Yuda, Benjamini ndi Efereimu ndiponso Manase amene anakhala mu Yerusalemu anali awa: Onani mutuwo |