1 Mbiri 9:2 - Buku Lopatulika2 Okhala m'dziko oyamba tsono, akukhala mwaomwao m'mizinda mwao, ndiwo Israele, ansembe, Alevi, ndi Antchito a m'kachisi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Okhala m'dziko oyamba tsono, akukhala mwaomwao m'midzi mwao, ndiwo Israele, ansembe, Alevi, ndi Anetini. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono Aisraele oyamba kukakhala m'maiko mwao ndi m'mizinda yao anali anthu wamba, ansembe, Alevi ndi atumiki a ku Nyumba ya Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Tsono anthu oyamba kukhala mʼmadera awo anali Aisraeli wamba, ansembe, Alevi ndi otumikira ku Nyumba ya Yehova. Onani mutuwo |