Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 8:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Saharaimu anabala ana ku dziko la Mowabu, atachotsa akazi ake Husimu ndi Baara.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Saharaimu anabala ana ku dziko la Mowabu, atachotsa akazi ake Husimu ndi Baara.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Saharaimu, atachotsa akazi ake Husimu ndi Baara, adakhala ndi ana m'dziko la Mowabu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Saharaimu anabereka ana ku Mowabu atalekana ndi akazi ake, Husimu ndi Baara.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 8:8
4 Mawu Ofanana  

Koma kwa ana a akazi ake aang'ono amene Abrahamu anali nao Abrahamu anapatsa mphatso, nawachotsa iwo kwa Isaki mwana wake, akali ndi moyo, kuti anke kum'mawa, ku dziko la kum'mawa.


natenga ndende Naamani, ndi Ahiya, ndi Gera, ndipo, anabala Uza, ndi Ahihudi.


Ndipo Hodesi mkazi wake anambalira Yobabu, ndi Zibiya, ndi Mesa, ndi Malikamu,


Ndipo masiku akuweruza oweruzawo munali njala m'dziko. Ndipo munthu wa ku Betelehemu ku Yuda anamuka nakagonera m'dziko la Mowabu, iyeyu, ndi mkazi wake, ndi ana ake aamuna awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa