Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 8:7 - Buku Lopatulika

7 natenga ndende Naamani, ndi Ahiya, ndi Gera, ndipo, anabala Uza, ndi Ahihudi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 natenga ndende Naamani, ndi Ahiya, ndi Gera, ndipo, anabala Uza, ndi Ahihudi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Anawo anali Namani, Ahiya ndi Gera. Gerayo amene anali bambo wake wa Uza ndi Ahihudi, ndiye adatsogolera anthu osamutsidwawo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Naamani, Ahiya ndi Gera, amene anawasamutsa ndipo anabereka Uza ndi Ahihudi.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 8:7
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana a Ehudi ndi awa: ndiwo akulu a nyumba za makolo ao a iwo okhala ku Geba, ndipo anawatenga ndende kunka ku Manahati,


Ndipo Saharaimu anabala ana ku dziko la Mowabu, atachotsa akazi ake Husimu ndi Baara.


ndi Ahiya mwana wa Ahitubi mbale wake wa Ikabodi, mwana wa Finehasi, mwana wa Eli, wansembe wa Yehova wa ku Silo, wovala efodi. Ndipo anthuwo sanadziwe kuti Yonatani wachoka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa