1 Mbiri 8:6 - Buku Lopatulika6 Ndi ana a Ehudi ndi awa: ndiwo akulu a nyumba za makolo ao a iwo okhala ku Geba, ndipo anawatenga ndende kunka ku Manahati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndi ana a Ehudi ndi awa: ndiwo akulu a nyumba za makolo ao a iwo okhala ku Geba, ndipo anawatenga ndende kunka ku Manahati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ana a Ehudi amene anali atsogoleri a mabanja okhala ku Geba, adachotsedwa kwaoko ndipo adakakhala ku Manahati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Zidzukulu za Ehudi, zimene zinali atsogoleri a mabanja a amene amakhala ku Geba ndipo zinasamutsidwa kupita ku Manahati zinali izi: Onani mutuwo |