1 Mbiri 8:13 - Buku Lopatulika13 ndi Beriya, ndi Sema; ndiwo akulu a nyumba za makolo a iwo okhala mu Ayaloni, amene anathawitsa okhala mu Gati; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 ndi Beriya, ndi Sema; ndiwo akulu a nyumba za makolo a iwo okhala m'Ayaloni, amene anathawitsa okhala m'Gati; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Beriya ndi Sema anali atsogoleri a mabanja okhala ku mzinda wa Aiyaloni. Iwowo adathaŵitsa nzika za ku Gati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 ndiponso Beriya ndi Sema, amene anali atsogoleri a mabanja a amene ankakhala ku Ayaloni ndipo anathamangitsa nzika za ku Gati. Onani mutuwo |