1 Mbiri 8:12 - Buku Lopatulika12 Ndi ana a Elipaala: Eberi, ndi Misamu, ndi Semedi, amene anamanga Ono, ndi Lodi ndi midzi yake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndi ana a Elipaala: Eberi, ndi Misamu, ndi Semedi, amene anamanga Ono, ndi Lodi ndi milaga yake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ana a Elipaala naŵa: Ebere, Misamu ndi Semedi. Semedi ndiye adamanga mizinda ya Ono ndi Lodi pamodzi ndi midzi yake yomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ana a Elipaala anali awa: Eberi, Misamu, Semedi (amene anamanga mizinda ya Ono ndi Lodi ndi midzi yake yozungulira) Onani mutuwo |