Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 8:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Benjamini anabala Bela mwana wake woyamba, Asibele wachiwiri, ndi Ahara wachitatu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Benjamini anabala Bela mwana wake woyamba, Asibele wachiwiri, ndi Ahara wachitatu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Benjamini adabereka Bela mwana wake wachisamba, Asibele mwana wake wachiŵiri, Ahara mwana wake wachitatu,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Benjamini anabereka Bela mwana wake woyamba, wachiwiri Asibeli, wachitatu Ahara,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 8:1
5 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Benjamini: Bela ndi Bekere, ndi Asibele, ndi Gera, ndi Naamani, ndi Ehi ndi Rosi, Mupimu ndi Hupimu, ndi Aridi.


Awa onse ndiwo ana a Asere, akulu a nyumba za makolo ao, ngwazi zosankhika ndi zamphamvu, akulu mwa akalonga. Oyesedwa mwa chibadwidwe chao otumikira kunkhondo ndiwo amuna zikwi makumi awiri mphambu zisanu ndi chimodzi.


Noha wachinai, ndi Rafa wachisanu.


Ana aamuna a Benjamini monga mwa mabanja ao ndiwo: Bela, ndiye kholo la banja la Abela; Asibele, ndiye kholo la banja la Aasibele; Ahiramu, ndiye kholo la banja la Aahiramu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa