1 Mbiri 7:7 - Buku Lopatulika7 Ndi ana a Bela: Eziboni, ndi Uzi, ndi Uziyele, ndi Yerimoti, ndi Iri, asanu; akulu a nyumba za makolo ao, ngwazi zamphamvu, owerengedwa m'mabuku a chibadwidwe zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza makumi atatu ndi anai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndi ana a Bela: Eziboni, ndi Uzi, ndi Uziyele, ndi Yerimoti, ndi Iri, asanu; akulu a nyumba za makolo ao, ngwazi zamphamvu, owerengedwa m'mabuku a chibadwidwe zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza makumi atatu ndi anai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ana a Bela naŵa: Eziboni, Uzi, Uziyele, Yerimoti ndi Iri, asanu, atsogoleri a mabanja a makolo ao, ankhondo amphamvu. Ndipo chiŵerengero chao potsata mibadwo yao chinali 22,034. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ana a Bela anali awa: Eziboni, Uzi, Uzieli, Yerimoti ndi Iri. Iwowa anali atsogoleri a mabanja awo ndipo onse pamodzi analipo asanu. Pa mndandanda wa mʼbado wawo panali anthu 22,034 odziwa kumenya nkhondo. Onani mutuwo |