Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 7:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo Refa anali mwana wake, ndi Resefi, ndi Tela mwana wake, ndi Tahani mwana wake,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo Refa anali mwana wake, ndi Resefi, ndi Tela mwana wake, ndi Tahani mwana wake,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Mwana wina wa Efuremu anali Refa, amene zidzukulu zake zinali izi: Resefi, Tela, Tahani,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Mwana wina wa Efereimu anali Refa amene zidzukulu zake zinali Resefu, Tela, Tahani,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 7:25
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mwana wake wamkazi ndiye Seera, amene anamanga Betehoroni wa kunsi, ndi Betehoroni wa kumtunda, ndi Uzeniseera.


Ladani mwana wake, Amihudi mwana wake, Elisama mwana wake,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa