Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 7:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo mwana wake wamkazi ndiye Seera, amene anamanga Betehoroni wa kunsi, ndi Betehoroni wa kumtunda, ndi Uzeniseera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo mwana wake wamkazi ndiye Seera, amene anamanga Betehoroni wa kunsi, ndi Betehoroni wa kumtunda, ndi Uzeniseera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Mwana wake wamkazi anali Seera, amene adamanga mzinda wa Betehoroni wakunsi ndi Betehoroni wakumtunda, kudzanso Uzeniseera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Mwana wake wamkazi anali Seera, amene anamanga mzinda wa Beti-Horoni Wakumunsi, Wakumtunda kudzanso Uzeni-Seera.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 7:24
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Solomoni anamanganso Gezere, ndi Betehoroni wakunsi,


Ndipo analowa kwa mkazi wake, naima iye, nabala mwana, namutcha dzina lake Beriya, popeza m'nyumba mwake mudaipa.


Ndipo Refa anali mwana wake, ndi Resefi, ndi Tela mwana wake, ndi Tahani mwana wake,


Anamanganso Betehoroni wa kumtunda, ndi Betehoroni wa kunsi, mizinda ya malinga yokhala nao malinga, zitseko, ndi mipiringidzo;


Ndipo Yehova anawamwaza pamaso pa Israele, ndipo anawakantha makanthidwe aakulu ku Gibiyoni, nawapirikitsa panjira yokwera pa Betehoroni, nawakantha mpaka Azeka, ndi mpaka Makeda.


natsikira kumadzulo kunka ku malire a Ayafileti, ku malire a Betehoroni wa kunsi, ndi ku Gezere; ndi matulukiro ake anali kunyanja.


Ndipo malire a ana a Efuremu, monga mwa mabanja ao, ndiwo: malire a cholowa chao kum'mawa ndiwo Ataroti-Adara, mpaka Betehoroni wa kumtunda;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa