1 Mbiri 7:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo mwana wake wamkazi ndiye Seera, amene anamanga Betehoroni wa kunsi, ndi Betehoroni wa kumtunda, ndi Uzeniseera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo mwana wake wamkazi ndiye Seera, amene anamanga Betehoroni wa kunsi, ndi Betehoroni wa kumtunda, ndi Uzeniseera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Mwana wake wamkazi anali Seera, amene adamanga mzinda wa Betehoroni wakunsi ndi Betehoroni wakumtunda, kudzanso Uzeniseera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Mwana wake wamkazi anali Seera, amene anamanga mzinda wa Beti-Horoni Wakumunsi, Wakumtunda kudzanso Uzeni-Seera. Onani mutuwo |