Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 7:18 - Buku Lopatulika

18 Ndi mlongo wake Hamoleketi anabala Isihodi, ndi Abiyezere, ndi Mala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndi mlongo wake Hamoleketi anabala Isihodi, ndi Abiyezere, ndi Mala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Mlongo wake Hamoleketi adabala Isihodi, Abiyezere ndi Mala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Mlongo wake Hamoleketi anabereka Isihodi, Abiezeri ndi Mahila.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 7:18
8 Mawu Ofanana  

Ndi mwana wa Ulamu: Bedani; ndiwo ana a Giliyadi mwana wa Makiri mwana wa Manase.


Ndi ana a Semida ndiwo Ahiyani, ndi Sekemu, ndi Liki, ndi Aniyamu.


Ana a Giliyadi ndiwo: Iyezere, ndiye kholo la banja la Aiyezere; Heleki, ndiye kholo la banja la Aheleki;


Ndipo maere anagwera ana ena otsala a Manase monga mwa mabanja ao; ana a Abiyezere ndi ana a Heleki, ndi ana a Asiriele, ndi ana a Sekemu ndi ana a Hefere, ndi ana a Semida; awa ndi ana aamuna a Manase mwana wa Yosefe, monga mwa mabanja ao.


Pamenepo anadza mthenga wa Yehova, nakhala patsinde pa thundu wokhala mu Ofura, wa Yowasi Mwabiyezere; ndi mwana wake Gideoni analikuomba tirigu m'mopondera mphesa, awabisire Amidiyani.


Pamenepo Gideoni anammangira Yehova guwa la nsembe pomwepo; nalitcha Yehova-ndiye-mtendere; likali mu Ofura wa Aabiyezere ndi pano pomwe.


Koma mzimu wa Yehova unavala Gideoni; naomba lipenga iye, ndi a banja la Abiyezere analalikidwa kumtsata iye.


Koma ananena nao, Ndachitanji tsopano monga inu? Kodi kukunkha mphesa kwa Efuremu sikuposa kutchera mphesa kwa Abiyezere?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa