1 Mbiri 7:12 - Buku Lopatulika12 Supimu yemwe ndi Hupimu ana a Iri, ndi Husimu mwana wa Aheri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Supimu yemwe ndi Hupimu ana a Iri, ndi Husimu mwana wa Aheri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Supimu ndi Hupimu anali ana a Iri, ndipo analinso a fuko ili. Husimu anali mwana wa Dan. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Asupi ndi Ahupi anali zidzukulu za Iri, ndipo Ahusimu anali zidzukulu za Aheri. Onani mutuwo |