Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 7:11 - Buku Lopatulika

11 Onsewa ndiwo ana a Yediyaele; ndiwo akulu a nyumba za makolo ao, ngwazi zamphamvu zikwi khumi mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana awiri akutuluka kugulu kunkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Onsewa ndiwo ana a Yediyaele; ndiwo akulu a nyumba za makolo ao, ngwazi zamphamvu zikwi khumi mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana awiri akutuluka kugulu kunkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Onseŵa anali ana a Yediyaele, atsogoleri a mabanja a makolo ao, ankhondo amphamvu 17,200, anthu okonzekera kumenya nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Ana onsewa a Yediaeli anali atsogoleri a mabanja. Analipo anthu 17,200 amene anali okonzeka kupita ku nkhondo.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 7:11
3 Mawu Ofanana  

Ndi mwana wa Yediyaele: Bilihani; ndi ana a Bilihani: Yeusi, ndi Benjamini, ndi Ehudi, ndi Kenana, ndi Zetani, ndi Tarisisi, ndi Ahisahara.


Supimu yemwe ndi Hupimu ana a Iri, ndi Husimu mwana wa Aheri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa