Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 7:1 - Buku Lopatulika

1 Ana a Isakara ndiwo Tola, ndi Puwa, Yasubu ndi Simironi; anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ana a Isakara ndiwo Tola, ndi Puwa, Yasubu ndi Simironi; anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Ana a Isakara naŵa: Tola, Puwa, Yasubu, ndi Simironi, anai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ana a Isakara anali awa: Tola, Puwa, Yasubu ndi Simironi ndipo onse analipo anayi.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 7:1
4 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Isakara: Tola ndi Puva, ndi Iyobu, ndi Simironi.


ndi Hesiboni ndi mabusa ake, ndi Yazere ndi mabusa ake.


Ndi ana a Tola: Uzi, ndi Refaya, ndi Yeriyele, ndi Yamai, ndi Ibisamu, ndi Semuele, akulu a nyumba za makolo; ao ndiwo a Tola, ngwazi zamphamvu, m'mibadwo yao; kuwerenga kwao, masiku a Davide ndiko zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza mazana asanu ndi limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa