Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 6:9 - Buku Lopatulika

9 ndi Ahimaazi anabala Azariya, ndi Azariya anabala Yohanani,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 ndi Ahimaazi anabala Azariya, ndi Azariya anabala Yohanani,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Ahimaazi adabereka Azariya, Azariya adabereka Yohanani,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ahimaazi anabereka Azariya, Azariya anabereka Yohanani,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 6:9
3 Mawu Ofanana  

ndi Yohanani anabala Azariya (ndiye amene anachita ntchito ya nsembe m'nyumba anaimanga Solomoni mu Yerusalemu),


ndi Ahitubi anabala Zadoki, ndi Zadoki anabala Ahimaazi,


Ndipo Azariya wansembe wamkulu wa nyumba ya Zadoki anamyankha, nati, Chiyambire anthu anabwera nazo zopereka kunyumba ya Yehova, tadya, takhuta, ndipo zitatsalira zambiri; pakuti Yehova anadalitsa anthu ake; ndipo siuku kuchuluka kwa chotsala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa