Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 6:2 - Buku Lopatulika

2 Ndi ana a Kohati: Amuramu, Izihara, ndi Hebroni, ndi Uziyele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndi ana a Kohati: Amuramu, Izihara, ndi Hebroni, ndi Uziyele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ana a Kohati naŵa: Amuramu, Izara, Hebroni ndi Uziyele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Ana a Kohati anali awa: Amramu, Izihari, Hebroni ndi Uzieli.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 6:2
7 Mawu Ofanana  

Ana a Kohati: Amuramu, Izihara, Hebroni, ndi Uziyele; anai.


A Ageresoni: Ladani ndi Simei.


Ana a Levi: Geresomo, Kohati, ndi Merari.


Eliyabu mwana wake, Yerohamu mwana wake, Elikana mwana wake.


Ndi ana a Amuramu: Aroni, ndi Mose, ndi Miriyamu. Ndi ana a Aroni: Nadabu, ndi Abihu, Eleazara, ndi Itamara.


Ndi ana aamuna a Kohati ndiwo: Amuramu ndi Izihara, ndi Hebroni, ndi Uziyele; ndipo zaka za moyo wa Kohati ndizo zana limodzi ndi makumi atatu ndi kudza zitatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa