Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 5:9 - Buku Lopatulika

9 ndi kum'mawa anakhala mpaka polowera kuchipululu kuyambira mtsinje wa Yufurate; pakuti zoweta zao zinachuluka m'dziko la Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 ndi kum'mawa anakhala mpaka polowera kuchipululu kuyambira mtsinje wa Yufurate; pakuti zoweta zao zinachuluka m'dziko la Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Iwowo adakhala kuvuma mpaka kukafika poloŵera m'chipululu cha mbali ina ya Yufurate, chifukwa chakuti ng'ombe zao zinali zitaswana kwambiri m'dziko la Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Iwo anakhala cha kummawa mpaka kukafika polowera mʼchipululu cha mbali ina ya Mtsinje wa Yufurate, chifukwa ziweto zawo zinaswana kwambiri mʼdziko la Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 5:9
1 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa