Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Mbiri 5:7 - Buku Lopatulika

7 Ndi abale ake monga mwa mabanja ao, powerenga chibadwidwe cha mibadwo yao: akulu ndiwo Yeiyele, ndi Zekariya,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndi abale ake monga mwa mabanja ao, powerenga chibadwidwe cha mibadwo yao: akulu ndiwo Yeiyele, ndi Zekariya,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Akuluakulu a fuko la Rubeni, potsata mndandanda wa maina ao, naŵa: mtsogoleri Yeiyele, Zekariya,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Abale awo mwa mabanja awo, potsata mndandanda wa mʼbado wawo, ndi awa: Yeiyeli, mtsogoleri, Zekariya,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 5:7
2 Mawu Ofanana  

Onsewo anawerengedwa monga mwa mabuku a chibadwidwe chao, masiku a Yotamu mfumu ya Yuda, ndi m'masiku a Yerobowamu mfumu ya Israele.


Beera mwana wake, amene Tigilati-Pilesere mfumu ya ku Asiriya anamtenga ndende; ndiye kalonga wa Arubeni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa