1 Mbiri 5:2 - Buku Lopatulika2 Pakuti Yuda anakula mphamvu mwa abale ake, ndi mtsogoleri anafuma kwa iyeyu, koma ukulu ngwa Yosefe); Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pakuti Yuda anakula mphamvu mwa abale ake, ndi mtsogoleri anafuma kwa iyeyu, koma ukulu ngwa Yosefe); Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Koma a fuko la Yuda anali amphamvu pakati pa mafuko a Israele, ndipo mfumu idachokera kwa iwowo, ngakhale kuti ukulu wa uchisamba unali wa Yosefe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 ndipo ngakhalenso Yuda anali wamphamvu kwambiri pakati pa abale ake, ndi kuti wolamulira anachokera mwa iye, ulemu wa mwana woyamba kubadwa unaperekedwa kwa Yosefe) Onani mutuwo |