1 Mbiri 5:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo anakhala mu Giliyadi mu Basani, ndi m'midzi yake, ndi podyetsa pake ponse pa Saroni, mpaka malire ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo anakhala m'Giliyadi m'Basani, ndi m'midzi yake, ndi podyetsa pake ponse pa Saroni, mpaka malire ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Iwowo adakhala m'midzi ya ku Giliyadi ndi ku Basani ndiponso ku mabusa onse a m'maiko a Saroni mpaka ku mapeto ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Fuko la Gadi linakhala ku Giliyadi, ku Basani ndi midzi yozugulira, madera onse a msipu a ku Saroni mpaka kumene amalekezera. Onani mutuwo |